×

Iye adati, “Chuma ichi chidapatsidwa kwa ine chifukwa cha nzeru zanga.” Kodi 28:78 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Qasas ⮕ (28:78) ayat 78 in Chichewa

28:78 Surah Al-Qasas ayat 78 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Qasas ayat 78 - القَصَص - Page - Juz 20

﴿قَالَ إِنَّمَآ أُوتِيتُهُۥ عَلَىٰ عِلۡمٍ عِندِيٓۚ أَوَلَمۡ يَعۡلَمۡ أَنَّ ٱللَّهَ قَدۡ أَهۡلَكَ مِن قَبۡلِهِۦ مِنَ ٱلۡقُرُونِ مَنۡ هُوَ أَشَدُّ مِنۡهُ قُوَّةٗ وَأَكۡثَرُ جَمۡعٗاۚ وَلَا يُسۡـَٔلُ عَن ذُنُوبِهِمُ ٱلۡمُجۡرِمُونَ ﴾
[القَصَص: 78]

Iye adati, “Chuma ichi chidapatsidwa kwa ine chifukwa cha nzeru zanga.” Kodi iye sadadziwe kuti Mulungu adaononga m’badwo wonse wa anthu amene adali ndi mphamvu zambiri ndiponso olemera kwambiri iye asanabadwe? Anthu ochita zoipa sadzafunsidwa za machimo awo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قال إنما أوتيته على علم عندي أو لم يعلم أن الله قد, باللغة نيانجا

﴿قال إنما أوتيته على علم عندي أو لم يعلم أن الله قد﴾ [القَصَص: 78]

Khaled Ibrahim Betala
“Adati: “Ndithu ndapatsidwa izi chifukwa cha kudziwa kwanga komwe ndili nako.” Kodi iye sadadziwe kuti Allah adawaononga anthu patsogolo pake omwe adali anyonga kwambiri kuposa iye, komanso osonkhanitsa chuma chambiri? Ndipo oipa sadzafunsidwa zolakwa zawo. (Allah akudziwa zonse za iwo)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek