×

Ndipo usamphatikize mulungu wina ndi Mulungu weniweni. Kulibe mulungu wina koma Iye 28:88 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Qasas ⮕ (28:88) ayat 88 in Chichewa

28:88 Surah Al-Qasas ayat 88 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Qasas ayat 88 - القَصَص - Page - Juz 20

﴿وَلَا تَدۡعُ مَعَ ٱللَّهِ إِلَٰهًا ءَاخَرَۘ لَآ إِلَٰهَ إِلَّا هُوَۚ كُلُّ شَيۡءٍ هَالِكٌ إِلَّا وَجۡهَهُۥۚ لَهُ ٱلۡحُكۡمُ وَإِلَيۡهِ تُرۡجَعُونَ ﴾
[القَصَص: 88]

Ndipo usamphatikize mulungu wina ndi Mulungu weniweni. Kulibe mulungu wina koma Iye yekha. Zinthu zonse ndi zakutha kupatula Iye yekha. Chake ndi chiweruzo ndipo kwa Iye ndi kumene mudzabwerera

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولا تدع مع الله إلها آخر لا إله إلا هو كل شيء, باللغة نيانجا

﴿ولا تدع مع الله إلها آخر لا إله إلا هو كل شيء﴾ [القَصَص: 88]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo usapemphe mulungu wina pa modzi ndi Allah. Palibe wopembedzedwa mwachoonadi koma Iye Yekha. Chinthu chilichonse chidzaonongeka kupatula Nkhope Yake. Ulamuliro (wazinthu zonse) uli kwa Iye ndipo kwa Iye ndi kumene mudzabwerera nonsenu
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek