×

Mulungu adakupambanitsani pa nkhondo ya ku Badr pamene inu mudali ofoka. Choncho 3:123 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:123) ayat 123 in Chichewa

3:123 Surah al-‘Imran ayat 123 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 123 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿وَلَقَدۡ نَصَرَكُمُ ٱللَّهُ بِبَدۡرٖ وَأَنتُمۡ أَذِلَّةٞۖ فَٱتَّقُواْ ٱللَّهَ لَعَلَّكُمۡ تَشۡكُرُونَ ﴾
[آل عِمران: 123]

Mulungu adakupambanitsani pa nkhondo ya ku Badr pamene inu mudali ofoka. Choncho opani Mulungu kwambiri kuti mukhale othokoza

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولقد نصركم الله ببدر وأنتم أذلة فاتقوا الله لعلكم تشكرون, باللغة نيانجا

﴿ولقد نصركم الله ببدر وأنتم أذلة فاتقوا الله لعلكم تشكرون﴾ [آل عِمران: 123]

Khaled Ibrahim Betala
“Allah adakupulumutsani pa (nkhondo) ya Badri pomwe inu munali ofooka (chifukwa chakuchepa ndi kusakhala ndi zida zokwanira). Choncho opani Allah kuti mumthokoze (nthawi zonse pa zomwe akukuchitirani)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek