×

Iwondiameneadanenazaabaleawoameneanafapamene iwo anakhala osapita ku nkhondo: Iwo akadatimvera ife, sakadaphedwa ayi. Nena: 3:168 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:168) ayat 168 in Chichewa

3:168 Surah al-‘Imran ayat 168 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 168 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿ٱلَّذِينَ قَالُواْ لِإِخۡوَٰنِهِمۡ وَقَعَدُواْ لَوۡ أَطَاعُونَا مَا قُتِلُواْۗ قُلۡ فَٱدۡرَءُواْ عَنۡ أَنفُسِكُمُ ٱلۡمَوۡتَ إِن كُنتُمۡ صَٰدِقِينَ ﴾
[آل عِمران: 168]

Iwondiameneadanenazaabaleawoameneanafapamene iwo anakhala osapita ku nkhondo: Iwo akadatimvera ife, sakadaphedwa ayi. Nena: “Dzichotsereni imfa imene ili pakati panu ngati zimene munena ndi zoona.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: الذين قالوا لإخوانهم وقعدوا لو أطاعونا ما قتلوا قل فادرءوا عن أنفسكم, باللغة نيانجا

﴿الذين قالوا لإخوانهم وقعدوا لو أطاعونا ما قتلوا قل فادرءوا عن أنفسكم﴾ [آل عِمران: 168]

Khaled Ibrahim Betala
“Iwo ndi amene adanena za abale awo pomwe iwo adakhala osapita ku nkhondo: “Akadatimvera, sibwenzi ataphedwa.” Nena: “Dzichotsereni imfa nokha, (kuti musafe) ngati mukunenadi zoona.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek