×

Ndipo kuti ayese anthu achinyengo ndipo iwo auzidwa kuti: “Bwerani kuti mumenye 3:167 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:167) ayat 167 in Chichewa

3:167 Surah al-‘Imran ayat 167 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 167 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿وَلِيَعۡلَمَ ٱلَّذِينَ نَافَقُواْۚ وَقِيلَ لَهُمۡ تَعَالَوۡاْ قَٰتِلُواْ فِي سَبِيلِ ٱللَّهِ أَوِ ٱدۡفَعُواْۖ قَالُواْ لَوۡ نَعۡلَمُ قِتَالٗا لَّٱتَّبَعۡنَٰكُمۡۗ هُمۡ لِلۡكُفۡرِ يَوۡمَئِذٍ أَقۡرَبُ مِنۡهُمۡ لِلۡإِيمَٰنِۚ يَقُولُونَ بِأَفۡوَٰهِهِم مَّا لَيۡسَ فِي قُلُوبِهِمۡۚ وَٱللَّهُ أَعۡلَمُ بِمَا يَكۡتُمُونَ ﴾
[آل عِمران: 167]

Ndipo kuti ayese anthu achinyengo ndipo iwo auzidwa kuti: “Bwerani kuti mumenye nkhondo mu njira ya Mulungu kapena kuti mudziteteze inu nokha.” Iwo adati: “Ngati ife tikadadziwa kuti kukhala nkhondo, ndithudi Ife tikadapita nanu.” Patsiku limeneli kusakhulupirira kwawo kudawayandikira kuposa chikhulupiriro. Iwo anali kunena ndi milomo yawo zinthu zomwe sizinali m’mitima yawo. Ndipo Mulungu amadziwa zimene iwo anali kubisa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وليعلم الذين نافقوا وقيل لهم تعالوا قاتلوا في سبيل الله أو ادفعوا, باللغة نيانجا

﴿وليعلم الذين نافقوا وقيل لهم تعالوا قاتلوا في سبيل الله أو ادفعوا﴾ [آل عِمران: 167]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndi kuwadziwitsa amene adachita uchiphamaso. Iwo adauzidwa: “Bwerani, menyani (nkhondo) pa njira ya Allah kapena mwatsekereze (adani kwa ife).” Adati: “Tikadadziwa kuti pali kumenyana, ndithudi, tikadakutsatani (koma kumeneko kuli kuphedwa kokhakokha basi).” Iwo tsiku limenelo adali pafupi ndikusakhulupirira kuposa chikhulupiliro (ngakhale kuti masiku onse amasonyeza Chisilamu mwa chiphamaso). Akunena ndi milomo yawo zomwe sizili m’mitima mwawo. Koma Allah akudziwa bwinobwino (zonse) zomwe akubisa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek