×

Koma iwo amene amaopa Mulungu, kuli minda yothiriridwa ndi madzi woyenda pansi 3:198 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:198) ayat 198 in Chichewa

3:198 Surah al-‘Imran ayat 198 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 198 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿لَٰكِنِ ٱلَّذِينَ ٱتَّقَوۡاْ رَبَّهُمۡ لَهُمۡ جَنَّٰتٞ تَجۡرِي مِن تَحۡتِهَا ٱلۡأَنۡهَٰرُ خَٰلِدِينَ فِيهَا نُزُلٗا مِّنۡ عِندِ ٱللَّهِۗ وَمَا عِندَ ٱللَّهِ خَيۡرٞ لِّلۡأَبۡرَارِ ﴾
[آل عِمران: 198]

Koma iwo amene amaopa Mulungu, kuli minda yothiriridwa ndi madzi woyenda pansi pake kumene adzakhalako mpaka kalekale, chisangalalo chochokera kwa Ambuye wawo. Ndithudi chimene chili ndi Mulungu ndi chabwino kwa anthu olungama

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لكن الذين اتقوا ربهم لهم جنات تجري من تحتها الأنهار خالدين فيها, باللغة نيانجا

﴿لكن الذين اتقوا ربهم لهم جنات تجري من تحتها الأنهار خالدين فيها﴾ [آل عِمران: 198]

Khaled Ibrahim Betala
“Koma amene aopa Mbuye wawo (potsatira zolamulidwa ndi kuleka zoletsedwa) adzapeza Minda yamtendere momwe mitsinje ikuyenda pansi (ndi patsogolo pake). Adzakhala m’menemo nthawi yaitali, ndi phwando lochokera kwa Allah. Ndipo zomwe zili kwa Allah nzabwino kwa anthu abwino (kuposa zosangalatsa za dziko lapansi)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek