×

“Inu mumasanduliza usiku kuti ukhale usana ndi usana kuti ukhale usiku. Inu 3:27 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:27) ayat 27 in Chichewa

3:27 Surah al-‘Imran ayat 27 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 27 - آل عِمران - Page - Juz 3

﴿تُولِجُ ٱلَّيۡلَ فِي ٱلنَّهَارِ وَتُولِجُ ٱلنَّهَارَ فِي ٱلَّيۡلِۖ وَتُخۡرِجُ ٱلۡحَيَّ مِنَ ٱلۡمَيِّتِ وَتُخۡرِجُ ٱلۡمَيِّتَ مِنَ ٱلۡحَيِّۖ وَتَرۡزُقُ مَن تَشَآءُ بِغَيۡرِ حِسَابٖ ﴾
[آل عِمران: 27]

“Inu mumasanduliza usiku kuti ukhale usana ndi usana kuti ukhale usiku. Inu mumatulutsa cha moyo kuchokera ku chakufa ndi chakufa kuchokera ku chamoyo. Inu mumapereka chuma ndi chakudya moolowa manja kwa aliyense amene Inu mwamufuna.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: تولج الليل في النهار وتولج النهار في الليل وتخرج الحي من الميت, باللغة نيانجا

﴿تولج الليل في النهار وتولج النهار في الليل وتخرج الحي من الميت﴾ [آل عِمران: 27]

Khaled Ibrahim Betala
“(Inu) mumalowetsa usiku mu usana (ndikukhala usana wautali monga m’nyengo yotentha). Ndipo mumalowetsa usana mu usiku (nkukhala usiku wautali monga m’nyengo yachisanu). Mumatulutsa cha moyo m’chakufa; ndipo mumatulutsa chakufa m’chamoyo. Ndipo mumapatsa rizq (chakudya) amene mwamfuna mopanda chiwerengero.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek