×

Nena: “Kaya mubisa zimene zili mumitima mwanu kapena muulula, zonse Mulungu akuzidziwa. 3:29 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:29) ayat 29 in Chichewa

3:29 Surah al-‘Imran ayat 29 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 29 - آل عِمران - Page - Juz 3

﴿قُلۡ إِن تُخۡفُواْ مَا فِي صُدُورِكُمۡ أَوۡ تُبۡدُوهُ يَعۡلَمۡهُ ٱللَّهُۗ وَيَعۡلَمُ مَا فِي ٱلسَّمَٰوَٰتِ وَمَا فِي ٱلۡأَرۡضِۗ وَٱللَّهُ عَلَىٰ كُلِّ شَيۡءٖ قَدِيرٞ ﴾
[آل عِمران: 29]

Nena: “Kaya mubisa zimene zili mumitima mwanu kapena muulula, zonse Mulungu akuzidziwa. Ndipo Iye amadziwa zonse zimene zili mlengalenga ndi zimene zili padziko lapansi. Ndipo Mulungu ali ndi mphamvu pa zinthu zonse.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل إن تخفوا ما في صدوركم أو تبدوه يعلمه الله ويعلم ما, باللغة نيانجا

﴿قل إن تخفوا ما في صدوركم أو تبدوه يعلمه الله ويعلم ما﴾ [آل عِمران: 29]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena: “Ngati mubisa zomwe zili m’zifuwa zanu, kapena kuzionetsa (poyera), Allah akuzidziwa. Iye akudziwa zonse zakumwamba ndi zapansi. Ndipo Allah Ngokhoza chilichonse.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek