×

Iye adati: “oh Ambuye wanga! Kodi ine ndingabereke mwana bwanji pamene sindidakhudzidwe 3:47 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:47) ayat 47 in Chichewa

3:47 Surah al-‘Imran ayat 47 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 47 - آل عِمران - Page - Juz 3

﴿قَالَتۡ رَبِّ أَنَّىٰ يَكُونُ لِي وَلَدٞ وَلَمۡ يَمۡسَسۡنِي بَشَرٞۖ قَالَ كَذَٰلِكِ ٱللَّهُ يَخۡلُقُ مَا يَشَآءُۚ إِذَا قَضَىٰٓ أَمۡرٗا فَإِنَّمَا يَقُولُ لَهُۥ كُن فَيَكُونُ ﴾
[آل عِمران: 47]

Iye adati: “oh Ambuye wanga! Kodi ine ndingabereke mwana bwanji pamene sindidakhudzidwe ndi mwamuna?” Iye adati: “Zidzakhala choncho, chifukwa Mulungu amalenga chimene afuna. Ndipo pamene afuna chinthu, Iye amangonena kwa icho, ‘Khala’ ndipo chimakhala.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قالت رب أنى يكون لي ولد ولم يمسسني بشر قال كذلك الله, باللغة نيانجا

﴿قالت رب أنى يكون لي ولد ولم يمسسني بشر قال كذلك الله﴾ [آل عِمران: 47]

Khaled Ibrahim Betala
“(Mariya) adati: “Mbuye wanga! Ndingakhale ndi mwana bwanji pomwe sadandikhudze munthu aliyense (wamwamuna)?” (Mngelo) adati: “Ndi momwemo. Allah amalenga chimene wafuna. Akafuna chinthu amanena kwa icho: ‘Chitika,’ ndipo chimachitikadi.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek