×

Kodi iwo saona kuti Mulungu amapereka moolowa manja kwa aliyense amene Iye 30:37 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ar-Rum ⮕ (30:37) ayat 37 in Chichewa

30:37 Surah Ar-Rum ayat 37 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ar-Rum ayat 37 - الرُّوم - Page - Juz 21

﴿أَوَلَمۡ يَرَوۡاْ أَنَّ ٱللَّهَ يَبۡسُطُ ٱلرِّزۡقَ لِمَن يَشَآءُ وَيَقۡدِرُۚ إِنَّ فِي ذَٰلِكَ لَأٓيَٰتٖ لِّقَوۡمٖ يُؤۡمِنُونَ ﴾
[الرُّوم: 37]

Kodi iwo saona kuti Mulungu amapereka moolowa manja kwa aliyense amene Iye wamufuna ndiponso zomupatsazochepa munthu yemwe wamufuna. Ndithudi mu chimenechi muli phunziro kwa anthu okhulupirira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أو لم يروا أن الله يبسط الرزق لمن يشاء ويقدر إن في, باللغة نيانجا

﴿أو لم يروا أن الله يبسط الرزق لمن يشاء ويقدر إن في﴾ [الرُّوم: 37]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi saona kuti Allah amamchulukitsira rizq yemwe wamfuna, ndi kumchepetsera (yemwe wamfuna)? Ndithu m’zimenezi, muli zisonyezo kwa anthu okhulupirira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek