×

Chimene mumapereka ngati chiongoladzanja kuti chionjezere chuma cha anthu, sichidzakhala ndi chionjezero 30:39 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ar-Rum ⮕ (30:39) ayat 39 in Chichewa

30:39 Surah Ar-Rum ayat 39 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ar-Rum ayat 39 - الرُّوم - Page - Juz 21

﴿وَمَآ ءَاتَيۡتُم مِّن رِّبٗا لِّيَرۡبُوَاْ فِيٓ أَمۡوَٰلِ ٱلنَّاسِ فَلَا يَرۡبُواْ عِندَ ٱللَّهِۖ وَمَآ ءَاتَيۡتُم مِّن زَكَوٰةٖ تُرِيدُونَ وَجۡهَ ٱللَّهِ فَأُوْلَٰٓئِكَ هُمُ ٱلۡمُضۡعِفُونَ ﴾
[الرُّوم: 39]

Chimene mumapereka ngati chiongoladzanja kuti chionjezere chuma cha anthu, sichidzakhala ndi chionjezero kwa Mulungu. Koma zopereka zimene mupereka ngati chaulere ndi cholinga chopeza madalitso a Mulungu ndi chimenechi chimene chidzaonjezeredwa kwambirimbiri

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وما آتيتم من ربا ليربو في أموال الناس فلا يربو عند الله, باللغة نيانجا

﴿وما آتيتم من ربا ليربو في أموال الناس فلا يربو عند الله﴾ [الرُّوم: 39]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo chuma chimene mukupatsana m’njira yamphatso kuti chichuluke m’chuma cha anthu, kwa Allah sichichuluka. Koma (chuma) chimene mukuchipereka m’njira ya Zakaat uku mukufuna chiyanjo cha Allah (chimachuluka). Iwowo ndi amene adzapeza mphoto yochuluka
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek