×

Motero Mulungu adzalanga amuna ndi akazi a chinyengo. Ndiponso amuna ndi akazi 33:73 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahzab ⮕ (33:73) ayat 73 in Chichewa

33:73 Surah Al-Ahzab ayat 73 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahzab ayat 73 - الأحزَاب - Page - Juz 22

﴿لِّيُعَذِّبَ ٱللَّهُ ٱلۡمُنَٰفِقِينَ وَٱلۡمُنَٰفِقَٰتِ وَٱلۡمُشۡرِكِينَ وَٱلۡمُشۡرِكَٰتِ وَيَتُوبَ ٱللَّهُ عَلَى ٱلۡمُؤۡمِنِينَ وَٱلۡمُؤۡمِنَٰتِۗ وَكَانَ ٱللَّهُ غَفُورٗا رَّحِيمَۢا ﴾
[الأحزَاب: 73]

Motero Mulungu adzalanga amuna ndi akazi a chinyengo. Ndiponso amuna ndi akazi opembedza mafano. Ndipo Mulungu adzakhululukira anthu onse okhululupirira, amuna ndi akazi. Mulungu ndi wokhululukira ndiponso mwini chisoni chosatha

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ليعذب الله المنافقين والمنافقات والمشركين والمشركات ويتوب الله على المؤمنين والمؤمنات وكان, باللغة نيانجا

﴿ليعذب الله المنافقين والمنافقات والمشركين والمشركات ويتوب الله على المؤمنين والمؤمنات وكان﴾ [الأحزَاب: 73]

Khaled Ibrahim Betala
“Kuti Allah adzawalange achiphamaso aamuna ndi aakazi, ndi opembedza mafano achimuna ndi achikazi ndi kuti adzawakhululukire okhulupirira achimuna ndi achikazi. Ndipo Allah Ngokhululuka kwabasi, Ngwachisoni chosatha
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek