×

Ndithudi kunali chizindikiro kwa onse a Saba m’chikhalidwe chawo. Minda iwiri ku 34:15 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Saba’ ⮕ (34:15) ayat 15 in Chichewa

34:15 Surah Saba’ ayat 15 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Saba’ ayat 15 - سَبإ - Page - Juz 22

﴿لَقَدۡ كَانَ لِسَبَإٖ فِي مَسۡكَنِهِمۡ ءَايَةٞۖ جَنَّتَانِ عَن يَمِينٖ وَشِمَالٖۖ كُلُواْ مِن رِّزۡقِ رَبِّكُمۡ وَٱشۡكُرُواْ لَهُۥۚ بَلۡدَةٞ طَيِّبَةٞ وَرَبٌّ غَفُورٞ ﴾
[سَبإ: 15]

Ndithudi kunali chizindikiro kwa onse a Saba m’chikhalidwe chawo. Minda iwiri ku dzanja lamanja ndi minda iwiri kudzanja lamanzere. Idyani zabwino zochokera kwa Ambuye wanu ndipo mumuyamike Iye. Kwa iye kuli dziko labwino ndiponso ndi Ambuye wokhululukira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لقد كان لسبإ في مسكنهم آية جنتان عن يمين وشمال كلوا من, باللغة نيانجا

﴿لقد كان لسبإ في مسكنهم آية جنتان عن يمين وشمال كلوا من﴾ [سَبإ: 15]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithu padali phunziro pa anthu a dziko la Saba mokhala mwawo: (Padali) minda iwiri, kumanja ndi kumanzere. (Tidati:) “Idyani zakudya zaulere zochokera kwa Mbuye wanu, ndipo mthokozeni. Mudzi wabwino ndi Mbuye Wokhululuka.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek