×

Nena, “oh inu akapolo anga amene mwakhulupirira! opani Ambuye wanu. Mphotho yokoma 39:10 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Az-Zumar ⮕ (39:10) ayat 10 in Chichewa

39:10 Surah Az-Zumar ayat 10 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Az-Zumar ayat 10 - الزُّمَر - Page - Juz 23

﴿قُلۡ يَٰعِبَادِ ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ ٱتَّقُواْ رَبَّكُمۡۚ لِلَّذِينَ أَحۡسَنُواْ فِي هَٰذِهِ ٱلدُّنۡيَا حَسَنَةٞۗ وَأَرۡضُ ٱللَّهِ وَٰسِعَةٌۗ إِنَّمَا يُوَفَّى ٱلصَّٰبِرُونَ أَجۡرَهُم بِغَيۡرِ حِسَابٖ ﴾
[الزُّمَر: 10]

Nena, “oh inu akapolo anga amene mwakhulupirira! opani Ambuye wanu. Mphotho yokoma ili kuwandikira iwo amene amachita zabwino m’dziko lino. Ndipo dziko la Mulungu lili ndi malo ambiri. Ndipo onse amene amapirira, ndithudi adzalandira mphotho yopanda malire.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل ياعباد الذين آمنوا اتقوا ربكم للذين أحسنوا في هذه الدنيا حسنة, باللغة نيانجا

﴿قل ياعباد الذين آمنوا اتقوا ربكم للذين أحسنوا في هذه الدنيا حسنة﴾ [الزُّمَر: 10]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena (kwa iwo mau Anga akuti): “E inu akapolo Anga amene mwakhulupirira! Muopeni Mbuye wanu. Ndithu amene achita zabwino zotsatira zake nzabwino padziko lapansi, ndipo dziko la Allah ndilophanuka. (Pirirani chifukwa chosiya midzi yanu ndi abale). Ndithu opirira adzalipidwa malipiro awo mokwana mopanda mulingo.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek