×

Ndithudi kumvera ndi kupembedza, ndi kwa Mulungu yekha ndipo iwo amene amasankha 39:3 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Az-Zumar ⮕ (39:3) ayat 3 in Chichewa

39:3 Surah Az-Zumar ayat 3 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Az-Zumar ayat 3 - الزُّمَر - Page - Juz 23

﴿أَلَا لِلَّهِ ٱلدِّينُ ٱلۡخَالِصُۚ وَٱلَّذِينَ ٱتَّخَذُواْ مِن دُونِهِۦٓ أَوۡلِيَآءَ مَا نَعۡبُدُهُمۡ إِلَّا لِيُقَرِّبُونَآ إِلَى ٱللَّهِ زُلۡفَىٰٓ إِنَّ ٱللَّهَ يَحۡكُمُ بَيۡنَهُمۡ فِي مَا هُمۡ فِيهِ يَخۡتَلِفُونَۗ إِنَّ ٱللَّهَ لَا يَهۡدِي مَنۡ هُوَ كَٰذِبٞ كَفَّارٞ ﴾
[الزُّمَر: 3]

Ndithudi kumvera ndi kupembedza, ndi kwa Mulungu yekha ndipo iwo amene amasankha ena kuti akhale owasamala m’malo mwa Mulungu amati, “Ife sitiwapembedza iwo ayi koma timafuna kuti iwo atifikitse pafupi ndi Mulungu.” Ndithudi Mulungu adzaweruza pa zonse zimene iwo amatsutsana. Ndithudi Mulungu satsogolera wabodza ndi wosakhulupirira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ألا لله الدين الخالص والذين اتخذوا من دونه أولياء ما نعبدهم إلا, باللغة نيانجا

﴿ألا لله الدين الخالص والذين اتخذوا من دونه أولياء ما نعبدهم إلا﴾ [الزُّمَر: 3]

Khaled Ibrahim Betala
“Dziwani kuti Allah Ngolandira mapemphero oyera, (opanda kuphatikizidwa ndi zina). Koma amene adzipangira athandizi kusiya Allah, (akumanena kuti): “Ife sitikuwapembedza awa, koma tikutero ndi cholinga choti atifikitse pafupi ndi Allah.” Ndithu Allah, adzaweruza pakati pawo (pakati pa okhulupirira Allah, ndi okana) pa zimene akusiyana. Ndithu Allah saongola amene ali wabodza; wokanira zedi (Allah)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek