×

Pamene vuto ligwa pa munthu, iye amatipempha Ife, koma pamene timuonetsa chifundo 39:49 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Az-Zumar ⮕ (39:49) ayat 49 in Chichewa

39:49 Surah Az-Zumar ayat 49 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Az-Zumar ayat 49 - الزُّمَر - Page - Juz 24

﴿فَإِذَا مَسَّ ٱلۡإِنسَٰنَ ضُرّٞ دَعَانَا ثُمَّ إِذَا خَوَّلۡنَٰهُ نِعۡمَةٗ مِّنَّا قَالَ إِنَّمَآ أُوتِيتُهُۥ عَلَىٰ عِلۡمِۭۚ بَلۡ هِيَ فِتۡنَةٞ وَلَٰكِنَّ أَكۡثَرَهُمۡ لَا يَعۡلَمُونَ ﴾
[الزُّمَر: 49]

Pamene vuto ligwa pa munthu, iye amatipempha Ife, koma pamene timuonetsa chifundo chathu, iye amati, “Izi zapatsidwa kwa ine chifukwa cha nzeru zanga.” Iyayi! Awa ndi mayesero chabe koma ambiri a iwo sadziwa chilichonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فإذا مس الإنسان ضر دعانا ثم إذا خولناه نعمة منا قال إنما, باللغة نيانجا

﴿فإذا مس الإنسان ضر دعانا ثم إذا خولناه نعمة منا قال إنما﴾ [الزُّمَر: 49]

Khaled Ibrahim Betala
“Pamene munthu mavuto amkhudza, amatipempha (uku ali wodzichepetsa); koma tikampatsa mtendere wochokera kwa Ife, amanena kuti: “Ndapatsidwa mtendere uwu chifukwa chakudziwa kwanga (njira zoupezera).” (Sichoncho) koma mtendere umenewu ndi mayeso; koma ambiri a iwo sadziwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek