×

Ndipo, ndithudi, zavumbulutsidwa kwa iwe ndi kwa iwo amene adalipo kale kuti, 39:65 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Az-Zumar ⮕ (39:65) ayat 65 in Chichewa

39:65 Surah Az-Zumar ayat 65 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Az-Zumar ayat 65 - الزُّمَر - Page - Juz 24

﴿وَلَقَدۡ أُوحِيَ إِلَيۡكَ وَإِلَى ٱلَّذِينَ مِن قَبۡلِكَ لَئِنۡ أَشۡرَكۡتَ لَيَحۡبَطَنَّ عَمَلُكَ وَلَتَكُونَنَّ مِنَ ٱلۡخَٰسِرِينَ ﴾
[الزُّمَر: 65]

Ndipo, ndithudi, zavumbulutsidwa kwa iwe ndi kwa iwo amene adalipo kale kuti, “Ndithudi ngati inu muphatikiza Mulungu ndi china chake, ndithudi, ntchito zanu zidzakhala zopanda phindu. Ndithudi inu mudzakhala m’gulu la anthu olephera.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولقد أوحي إليك وإلى الذين من قبلك لئن أشركت ليحبطن عملك ولتكونن, باللغة نيانجا

﴿ولقد أوحي إليك وإلى الذين من قبلك لئن أشركت ليحبطن عملك ولتكونن﴾ [الزُّمَر: 65]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo ndithu kwavumbulutsidwa kwa iwe, ndi kwa amene adalipo patsogolo pako (mawu awa:) “Ngati umphatikiza (Allah ndi milungu yabodza), ndithu ntchito zako zionongeka, ndipo ukhala mwa oluza (otaika).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek