×

Iye akuwalonjeza ndi kuwakhulupiritsa zinthu zopanda pake ndipo malonjezo a Satana si 4:120 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:120) ayat 120 in Chichewa

4:120 Surah An-Nisa’ ayat 120 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 120 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿يَعِدُهُمۡ وَيُمَنِّيهِمۡۖ وَمَا يَعِدُهُمُ ٱلشَّيۡطَٰنُ إِلَّا غُرُورًا ﴾
[النِّسَاء: 120]

Iye akuwalonjeza ndi kuwakhulupiritsa zinthu zopanda pake ndipo malonjezo a Satana si ena koma chinyengo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: يعدهم ويمنيهم وما يعدهم الشيطان إلا غرورا, باللغة نيانجا

﴿يعدهم ويمنيهم وما يعدهم الشيطان إلا غرورا﴾ [النِّسَاء: 120]

Khaled Ibrahim Betala
“(Satana) akuwalonjeza ndikuwapatsa chiyembekezo (pa zinthu zomwe sizingachitike). Ndithudi, satana sawalonjeza china koma chinyengo basi
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek