×

Ndipo aliyense amene amachita ntchito zabwino, mwamuna kapena mkazi, ndipo ndi wokhulupirira, 4:124 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:124) ayat 124 in Chichewa

4:124 Surah An-Nisa’ ayat 124 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 124 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿وَمَن يَعۡمَلۡ مِنَ ٱلصَّٰلِحَٰتِ مِن ذَكَرٍ أَوۡ أُنثَىٰ وَهُوَ مُؤۡمِنٞ فَأُوْلَٰٓئِكَ يَدۡخُلُونَ ٱلۡجَنَّةَ وَلَا يُظۡلَمُونَ نَقِيرٗا ﴾
[النِّسَاء: 124]

Ndipo aliyense amene amachita ntchito zabwino, mwamuna kapena mkazi, ndipo ndi wokhulupirira, ameneyo ndiye adzalowa ku Paradiso ndipo sadzaponderezedwa ngakhale pang’ono

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ومن يعمل من الصالحات من ذكر أو أنثى وهو مؤمن فأولئك يدخلون, باللغة نيانجا

﴿ومن يعمل من الصالحات من ذكر أو أنثى وهو مؤمن فأولئك يدخلون﴾ [النِّسَاء: 124]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo amene angachite ntchito zabwino, mwamuna kapena mkazi, pomwe iye ali wokhulupirira, iwo ndiamene adzalowa ku Munda wamtendere. Ndipo sadzaponderezedwa pa chilichonse, ngakhale chochepetsetsa kwambiri ngati kamphako ka nthangala ya tende
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek