×

Alipo wina pakati panu amene adzatsalira m’mbuyo. Amene ngati choipa chioneka kwa 4:72 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:72) ayat 72 in Chichewa

4:72 Surah An-Nisa’ ayat 72 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 72 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿وَإِنَّ مِنكُمۡ لَمَن لَّيُبَطِّئَنَّ فَإِنۡ أَصَٰبَتۡكُم مُّصِيبَةٞ قَالَ قَدۡ أَنۡعَمَ ٱللَّهُ عَلَيَّ إِذۡ لَمۡ أَكُن مَّعَهُمۡ شَهِيدٗا ﴾
[النِّسَاء: 72]

Alipo wina pakati panu amene adzatsalira m’mbuyo. Amene ngati choipa chioneka kwa inu amanena kuti: “Ndithudi Mulungu wandionetsera ine chifundo chifukwa sindinali nawo.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإن منكم لمن ليبطئن فإن أصابتكم مصيبة قال قد أنعم الله علي, باللغة نيانجا

﴿وإن منكم لمن ليبطئن فإن أصابتكم مصيبة قال قد أنعم الله علي﴾ [النِّسَاء: 72]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo ndithu alipo ena mwa inu otsalira m’mbuyo sapita ku nkhondo, (ndiponso amaletsa anzawo). Ngati vuto litakupezani, (yense wa iwo) amanena: “Allah wandichitira chisomo posakhala m’gulu lawo kumeneko.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek