×

Ndithudi iwo amene sakhulupirira adzamva mkuwo ukuti, “Ndithudi mkwiyo wa Mulungu pa 40:10 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ghafir ⮕ (40:10) ayat 10 in Chichewa

40:10 Surah Ghafir ayat 10 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ghafir ayat 10 - غَافِر - Page - Juz 24

﴿إِنَّ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ يُنَادَوۡنَ لَمَقۡتُ ٱللَّهِ أَكۡبَرُ مِن مَّقۡتِكُمۡ أَنفُسَكُمۡ إِذۡ تُدۡعَوۡنَ إِلَى ٱلۡإِيمَٰنِ فَتَكۡفُرُونَ ﴾
[غَافِر: 10]

Ndithudi iwo amene sakhulupirira adzamva mkuwo ukuti, “Ndithudi mkwiyo wa Mulungu pa inu ndi waukulu kuposa chidani chimene inuyo mumadzionetsera nokha poona kuti munali kuitanidwa kuti mukhulupirire koma inu munali kukana.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن الذين كفروا ينادون لمقت الله أكبر من مقتكم أنفسكم إذ تدعون, باللغة نيانجا

﴿إن الذين كفروا ينادون لمقت الله أكبر من مقتكم أنفسكم إذ تدعون﴾ [غَافِر: 10]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithu amene akanira adzaitanidwa (ndi kuuzidwa kuti): “Mkwiyo wa Allah pa inu udali waukulu kuposa mkwiyo wanu pa mitima yanu (yomwe yakulowetsani ku chilango) pamene mudali kuitanidwa ku chikhulupiliro, (ku Chisilamu); ndipo mudali kukanira.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek