×

Ndi Mulungu amene adalenga usiku kuti inu muzipumula ndi usana kuti ukupatseni 40:61 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ghafir ⮕ (40:61) ayat 61 in Chichewa

40:61 Surah Ghafir ayat 61 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ghafir ayat 61 - غَافِر - Page - Juz 24

﴿ٱللَّهُ ٱلَّذِي جَعَلَ لَكُمُ ٱلَّيۡلَ لِتَسۡكُنُواْ فِيهِ وَٱلنَّهَارَ مُبۡصِرًاۚ إِنَّ ٱللَّهَ لَذُو فَضۡلٍ عَلَى ٱلنَّاسِ وَلَٰكِنَّ أَكۡثَرَ ٱلنَّاسِ لَا يَشۡكُرُونَ ﴾
[غَافِر: 61]

Ndi Mulungu amene adalenga usiku kuti inu muzipumula ndi usana kuti ukupatseni kuwala. Ndithudi Mulungu amaonetsa chisomo chake kwa anthu koma anthu ambiri sathokoza ayi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: الله الذي جعل لكم الليل لتسكنوا فيه والنهار مبصرا إن الله لذو, باللغة نيانجا

﴿الله الذي جعل لكم الليل لتسكنوا فيه والنهار مبصرا إن الله لذو﴾ [غَافِر: 61]

Khaled Ibrahim Betala
“Allah ndi Yemwe adakupangirani usiku kuti mupumule mmenemo, ndi usana kukhala wounika (kuti muthe kuchita ntchito zanu). Ndithu Allah ndi Mwini kupereka ufulu kwa anthu. Koma anthu ambiri sathokoza
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek