×

Pamene Atumwi awo adadza kwa iwo ndi zizindikiro zooneka, iwo adadzitama chifukwa 40:83 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ghafir ⮕ (40:83) ayat 83 in Chichewa

40:83 Surah Ghafir ayat 83 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ghafir ayat 83 - غَافِر - Page - Juz 24

﴿فَلَمَّا جَآءَتۡهُمۡ رُسُلُهُم بِٱلۡبَيِّنَٰتِ فَرِحُواْ بِمَا عِندَهُم مِّنَ ٱلۡعِلۡمِ وَحَاقَ بِهِم مَّا كَانُواْ بِهِۦ يَسۡتَهۡزِءُونَ ﴾
[غَافِر: 83]

Pamene Atumwi awo adadza kwa iwo ndi zizindikiro zooneka, iwo adadzitama chifukwa cha nzeru zimene adali nazo. Ndipo chimene anali kutsutsa chidagwa pa iwo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فلما جاءتهم رسلهم بالبينات فرحوا بما عندهم من العلم وحاق بهم ما, باللغة نيانجا

﴿فلما جاءتهم رسلهم بالبينات فرحوا بما عندهم من العلم وحاق بهم ما﴾ [غَافِر: 83]

Khaled Ibrahim Betala
“Koma pamene atumiki awo adawadzera ndi zisonyezo zoonekera, adakondwera ndi kudziwa komwe adali nako, (ndipo sadalabadire zomwe atumiki adadza nazo). Choncho zidawazinga zimene adali kuzichitira chipongwe
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek