×

Ndipo iwo amati, “Mitima yathu ndi yokutidwa ku zimene iwe uli kutiitanira 41:5 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Fussilat ⮕ (41:5) ayat 5 in Chichewa

41:5 Surah Fussilat ayat 5 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Fussilat ayat 5 - فُصِّلَت - Page - Juz 24

﴿وَقَالُواْ قُلُوبُنَا فِيٓ أَكِنَّةٖ مِّمَّا تَدۡعُونَآ إِلَيۡهِ وَفِيٓ ءَاذَانِنَا وَقۡرٞ وَمِنۢ بَيۡنِنَا وَبَيۡنِكَ حِجَابٞ فَٱعۡمَلۡ إِنَّنَا عَٰمِلُونَ ﴾
[فُصِّلَت: 5]

Ndipo iwo amati, “Mitima yathu ndi yokutidwa ku zimene iwe uli kutiitanira ndipo makutu athu ndi ogontha ndipo chotchinga chili pakati pathu ndi iwe kotero iwe gwira ntchito yako ndipo nafenso tili kugwira yathu.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وقالوا قلوبنا في أكنة مما تدعونا إليه وفي آذاننا وقر ومن بيننا, باللغة نيانجا

﴿وقالوا قلوبنا في أكنة مما تدعونا إليه وفي آذاننا وقر ومن بيننا﴾ [فُصِّلَت: 5]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo akunena (kuti): “Mitima yathu (yaphimbidwa) m’zivindikiro, ku zomwe ukutiitanirazo, ndipo m’makutu mwathu muli kulemera kwa ugonthi; choncho pakati pathu ndi pakati pa iwe pali chotsekereza (chotchinga); tero chita (zakozo); nafe tichita (zathu; aliyense wa ife asalowelere za mnzake).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek