×

Nena, “Ine ndine munthu monga inu nomwe. Koma zavumbulutsidwa kwa ine kuti 41:6 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Fussilat ⮕ (41:6) ayat 6 in Chichewa

41:6 Surah Fussilat ayat 6 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Fussilat ayat 6 - فُصِّلَت - Page - Juz 24

﴿قُلۡ إِنَّمَآ أَنَا۠ بَشَرٞ مِّثۡلُكُمۡ يُوحَىٰٓ إِلَيَّ أَنَّمَآ إِلَٰهُكُمۡ إِلَٰهٞ وَٰحِدٞ فَٱسۡتَقِيمُوٓاْ إِلَيۡهِ وَٱسۡتَغۡفِرُوهُۗ وَوَيۡلٞ لِّلۡمُشۡرِكِينَ ﴾
[فُصِّلَت: 6]

Nena, “Ine ndine munthu monga inu nomwe. Koma zavumbulutsidwa kwa ine kuti Mulungu wanu ndi mmodzi yekha kotero tsatirani njira yoyenera yopita kwa Iye ndipo pemphani chikhululukiro chake. Tsoka kwa iwo amene amafanizira milungu ina ndi Mulungu weniweni.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل إنما أنا بشر مثلكم يوحى إلي أنما إلهكم إله واحد فاستقيموا, باللغة نيانجا

﴿قل إنما أنا بشر مثلكم يوحى إلي أنما إلهكم إله واحد فاستقيموا﴾ [فُصِّلَت: 6]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena: “Ndithu, ine ndi munthu monga inu; kukuvumbulutsidwa kwa ine (kuchokera kwa Allah) kuti ndithu Mulungu wanu ndi Mulungu Mmodzi; choncho lungamani kwa Iye ndipo mpempheni chikhululuko (pa zimene mwakhala mukumchimwira)” Ndipo kuonongeka kwakukulu kuli pa ophatikiza (Allah ndi zinthu zina)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek