×

Ndipo Mulungu adalenga kumwamba ndi dziko lapansi mwachoonadi kuti mzimu uliwonse ukhoza 45:22 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Jathiyah ⮕ (45:22) ayat 22 in Chichewa

45:22 Surah Al-Jathiyah ayat 22 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Jathiyah ayat 22 - الجاثِية - Page - Juz 25

﴿وَخَلَقَ ٱللَّهُ ٱلسَّمَٰوَٰتِ وَٱلۡأَرۡضَ بِٱلۡحَقِّ وَلِتُجۡزَىٰ كُلُّ نَفۡسِۭ بِمَا كَسَبَتۡ وَهُمۡ لَا يُظۡلَمُونَ ﴾
[الجاثِية: 22]

Ndipo Mulungu adalenga kumwamba ndi dziko lapansi mwachoonadi kuti mzimu uliwonse ukhoza kupeza dipo lake molingana ndi zimene udachita ndipo palibe amene adzaponderezedwa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وخلق الله السموات والأرض بالحق ولتجزى كل نفس بما كسبت وهم لا, باللغة نيانجا

﴿وخلق الله السموات والأرض بالحق ولتجزى كل نفس بما كسبت وهم لا﴾ [الجاثِية: 22]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo Allah adalenga thambo ndi nthaka moona ndi kuti mzimu uliwonse ulipidwe zimene udadzichitira, (zoipa kapena zabwino) ndipo iwo sadzaponderezedwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek