×

Ndipo iwo amati, “Kulibe china chilichonse kupatula moyo wathu wa pa dziko 45:24 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Jathiyah ⮕ (45:24) ayat 24 in Chichewa

45:24 Surah Al-Jathiyah ayat 24 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Jathiyah ayat 24 - الجاثِية - Page - Juz 25

﴿وَقَالُواْ مَا هِيَ إِلَّا حَيَاتُنَا ٱلدُّنۡيَا نَمُوتُ وَنَحۡيَا وَمَا يُهۡلِكُنَآ إِلَّا ٱلدَّهۡرُۚ وَمَا لَهُم بِذَٰلِكَ مِنۡ عِلۡمٍۖ إِنۡ هُمۡ إِلَّا يَظُنُّونَ ﴾
[الجاثِية: 24]

Ndipo iwo amati, “Kulibe china chilichonse kupatula moyo wathu wa pa dziko lapansi. Ife timakhala ndi moyo ndipo timafa ndipo palibe chimene chimationonga ife koma nthawi yokha ndiyo.” Ndipo iwo sadziwa chilichonse cha izo koma amangonena zongoganiza

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وقالوا ما هي إلا حياتنا الدنيا نموت ونحيا وما يهلكنا إلا الدهر, باللغة نيانجا

﴿وقالوا ما هي إلا حياتنا الدنيا نموت ونحيا وما يهلكنا إلا الدهر﴾ [الجاثِية: 24]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo (okanira kuuka ku imfa) adanena: “Kulibe (moyo wina) koma moyo wathu womwewu wa padziko lapansi; timafa ndi kukhala ndi moyo; palibe chikutiononga koma nthawi basi.” Koma iwo alibe kudziwa pa zimene akunenazo; akungoganizira chabe
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek