×

Nanga ndi chifukwa chiyani sadathandizidwe ndi iwo amene anali kuwapembedza ngati milungu 46:28 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahqaf ⮕ (46:28) ayat 28 in Chichewa

46:28 Surah Al-Ahqaf ayat 28 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahqaf ayat 28 - الأحقَاف - Page - Juz 26

﴿فَلَوۡلَا نَصَرَهُمُ ٱلَّذِينَ ٱتَّخَذُواْ مِن دُونِ ٱللَّهِ قُرۡبَانًا ءَالِهَةَۢۖ بَلۡ ضَلُّواْ عَنۡهُمۡۚ وَذَٰلِكَ إِفۡكُهُمۡ وَمَا كَانُواْ يَفۡتَرُونَ ﴾
[الأحقَاف: 28]

Nanga ndi chifukwa chiyani sadathandizidwe ndi iwo amene anali kuwapembedza ngati milungu yoonjezera pa Mulungu weniweni ndi cholinga chakuti iwabweretse kufupi ndi Mulungu? Iyayi. Iyo idawasiya padzuwa. Ndipo ilo linali bodza lomwe iwo anali kupeka

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فلولا نصرهم الذين اتخذوا من دون الله قربانا آلهة بل ضلوا عنهم, باللغة نيانجا

﴿فلولا نصرهم الذين اتخذوا من دون الله قربانا آلهة بل ضلوا عنهم﴾ [الأحقَاف: 28]

Khaled Ibrahim Betala
“Chifukwa chiyani siidawapulumutse milungu imene adaipangayo kusiya Allah kuti iwayandikitse kwa Iye (Allah)? Koma idasoweka kwa iwo (pomwe iwo adali pamavuto ofuna kulandira chithandizo). Ndipo zimenezo ndizo zotsatira zabodza lawo ndi zomwe adali kupeka
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek