×

Kodi iwo akudikira china kuposa Ola kuti lidze kwa iwo mwadzidzidzi? Koma 47:18 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Muhammad ⮕ (47:18) ayat 18 in Chichewa

47:18 Surah Muhammad ayat 18 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Muhammad ayat 18 - مُحمد - Page - Juz 26

﴿فَهَلۡ يَنظُرُونَ إِلَّا ٱلسَّاعَةَ أَن تَأۡتِيَهُم بَغۡتَةٗۖ فَقَدۡ جَآءَ أَشۡرَاطُهَاۚ فَأَنَّىٰ لَهُمۡ إِذَا جَآءَتۡهُمۡ ذِكۡرَىٰهُمۡ ﴾
[مُحمد: 18]

Kodi iwo akudikira china kuposa Ola kuti lidze kwa iwo mwadzidzidzi? Koma zizindikiro zina zadza kale, ndipo chitadza pa iwo, kodi iwo adzapindula chiyani ndi chikumbutso

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فهل ينظرون إلا الساعة أن تأتيهم بغتة فقد جاء أشراطها فأنى لهم, باللغة نيانجا

﴿فهل ينظرون إلا الساعة أن تأتيهم بغتة فقد جاء أشراطها فأنى لهم﴾ [مُحمد: 18]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi pali chimene akuyembekezera posakhala tsiku lachiweruziro limene liwadzere mwadzidzidzi (uku iwo ali otanganidwa ndi zam’dziko)? Ndithu zizindikiro zake zadza kale; kodi kudzawapindulira chiyani kukumbuka kwawo likadzawadzera (tsikulo)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek