×

Motero dziwani kuti kulibe mulungu wina koma Mulungu weniweni ndipo pempha chikhululukiro 47:19 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Muhammad ⮕ (47:19) ayat 19 in Chichewa

47:19 Surah Muhammad ayat 19 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Muhammad ayat 19 - مُحمد - Page - Juz 26

﴿فَٱعۡلَمۡ أَنَّهُۥ لَآ إِلَٰهَ إِلَّا ٱللَّهُ وَٱسۡتَغۡفِرۡ لِذَنۢبِكَ وَلِلۡمُؤۡمِنِينَ وَٱلۡمُؤۡمِنَٰتِۗ وَٱللَّهُ يَعۡلَمُ مُتَقَلَّبَكُمۡ وَمَثۡوَىٰكُمۡ ﴾
[مُحمد: 19]

Motero dziwani kuti kulibe mulungu wina koma Mulungu weniweni ndipo pempha chikhululukiro chako ndi cha amuna ndi akazi amene amakhulupirira. Ndipo Mulungu amadziwa mmene inu mumayendera ndi mmene mumakhalira m’nyumba zanu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فاعلم أنه لا إله إلا الله واستغفر لذنبك وللمؤمنين والمؤمنات والله يعلم, باللغة نيانجا

﴿فاعلم أنه لا إله إلا الله واستغفر لذنبك وللمؤمنين والمؤمنات والله يعلم﴾ [مُحمد: 19]

Khaled Ibrahim Betala
“Dziwa kuti palibe wompembedza m’choonadi koma Allah, ndipo pempha chikhululuko pa zolakwa zako ndi zolakwa za okhulupirira aamuna ndi aakazi; ndipo Allah akudziwa malo anu opita ndi kubwera ndi malo anu Wokhazikika
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek