×

Ndithudi Ife tidzakuyesani mpaka pamene tiyesa onse amene amalimbikira kwambiri ndi iwo 47:31 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Muhammad ⮕ (47:31) ayat 31 in Chichewa

47:31 Surah Muhammad ayat 31 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Muhammad ayat 31 - مُحمد - Page - Juz 26

﴿وَلَنَبۡلُوَنَّكُمۡ حَتَّىٰ نَعۡلَمَ ٱلۡمُجَٰهِدِينَ مِنكُمۡ وَٱلصَّٰبِرِينَ وَنَبۡلُوَاْ أَخۡبَارَكُمۡ ﴾
[مُحمد: 31]

Ndithudi Ife tidzakuyesani mpaka pamene tiyesa onse amene amalimbikira kwambiri ndi iwo amene opirira ndipo Ife tidzayesa ntchito zanu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولنبلونكم حتى نعلم المجاهدين منكم والصابرين ونبلوا أخباركم, باللغة نيانجا

﴿ولنبلونكم حتى نعلم المجاهدين منكم والصابرين ونبلوا أخباركم﴾ [مُحمد: 31]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo ndithu tikuyesani mayeso mpaka tiwaonetsere poyera (adziwike) amene akumenya nkhondo mwa inu (chifukwa cha dini) ndi opirira (pamavuto); ndi kuzionetsera poyera nkhani zanu (zochita zanu)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek