×

Ife tikadafuna tikadakuonetsa iwe ndipo iwe ukadawadziwa chifukwa cha zizindikiro zawo ndipo, 47:30 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Muhammad ⮕ (47:30) ayat 30 in Chichewa

47:30 Surah Muhammad ayat 30 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Muhammad ayat 30 - مُحمد - Page - Juz 26

﴿وَلَوۡ نَشَآءُ لَأَرَيۡنَٰكَهُمۡ فَلَعَرَفۡتَهُم بِسِيمَٰهُمۡۚ وَلَتَعۡرِفَنَّهُمۡ فِي لَحۡنِ ٱلۡقَوۡلِۚ وَٱللَّهُ يَعۡلَمُ أَعۡمَٰلَكُمۡ ﴾
[مُحمد: 30]

Ife tikadafuna tikadakuonetsa iwe ndipo iwe ukadawadziwa chifukwa cha zizindikiro zawo ndipo, ndithudi, udzawadziwa chifukwa cha mayankhulidwe awo. Mulungu amadziwa ntchito zanu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولو نشاء لأريناكهم فلعرفتهم بسيماهم ولتعرفنهم في لحن القول والله يعلم أعمالكم, باللغة نيانجا

﴿ولو نشاء لأريناكهم فلعرفتهم بسيماهم ولتعرفنهم في لحن القول والله يعلم أعمالكم﴾ [مُحمد: 30]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo tikadafuna tikadakuonetsa iwo (amene akuchitira kaduka Chisilamu) ndipo ukadawadziwa ndi zizindikiro zawo. Koma ndithu uwadziwa m’kayankhulidwe (kawo) kokometsa ndipo Allah akudziwa zochita zanu zonse
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek