×

Mulungu wakulonjeza katundu wambiri amene udzalandira ndipo wakupatsiratu, ndipo Iye wamanga manja 48:20 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Fath ⮕ (48:20) ayat 20 in Chichewa

48:20 Surah Al-Fath ayat 20 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Fath ayat 20 - الفَتح - Page - Juz 26

﴿وَعَدَكُمُ ٱللَّهُ مَغَانِمَ كَثِيرَةٗ تَأۡخُذُونَهَا فَعَجَّلَ لَكُمۡ هَٰذِهِۦ وَكَفَّ أَيۡدِيَ ٱلنَّاسِ عَنكُمۡ وَلِتَكُونَ ءَايَةٗ لِّلۡمُؤۡمِنِينَ وَيَهۡدِيَكُمۡ صِرَٰطٗا مُّسۡتَقِيمٗا ﴾
[الفَتح: 20]

Mulungu wakulonjeza katundu wambiri amene udzalandira ndipo wakupatsiratu, ndipo Iye wamanga manja ya anthu kuti asakukhudze, kuti chikhale chizindikiro kwa anthu okhulupirira ndipo kuti Iye akutsogolere ku njira yoyenera

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وعدكم الله مغانم كثيرة تأخذونها فعجل لكم هذه وكف أيدي الناس عنكم, باللغة نيانجا

﴿وعدكم الله مغانم كثيرة تأخذونها فعجل لكم هذه وكف أيدي الناس عنكم﴾ [الفَتح: 20]

Khaled Ibrahim Betala
“Allah wakulonjezani zofunkha zambiri zapankhondo (zomwe) mudzazitenga, ndipo wachita changu kukupatsani izi, (zinazo asanakupatseni). Ndipo watsekereza manja a anthu pa inu (kuti asakumenyeni). Ndi kuti chikhale chisonyezo cha okhulupirira (amene akudza pambuyo panu), ndi kuti akuongolereni kunjira yolunjika
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek