×

Ndipo ndiye amene adamanga manja awo kuti asakukhudzeni inu ndipo manja anu 48:24 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Fath ⮕ (48:24) ayat 24 in Chichewa

48:24 Surah Al-Fath ayat 24 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Fath ayat 24 - الفَتح - Page - Juz 26

﴿وَهُوَ ٱلَّذِي كَفَّ أَيۡدِيَهُمۡ عَنكُمۡ وَأَيۡدِيَكُمۡ عَنۡهُم بِبَطۡنِ مَكَّةَ مِنۢ بَعۡدِ أَنۡ أَظۡفَرَكُمۡ عَلَيۡهِمۡۚ وَكَانَ ٱللَّهُ بِمَا تَعۡمَلُونَ بَصِيرًا ﴾
[الفَتح: 24]

Ndipo ndiye amene adamanga manja awo kuti asakukhudzeni inu ndipo manja anu kuti asawakhudze iwo m’kati mwa Makka pamene Iye adakupambanitsani inu. Ndipo Mulungu amaona zonse zimene mumachita

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وهو الذي كف أيديهم عنكم وأيديكم عنهم ببطن مكة من بعد أن, باللغة نيانجا

﴿وهو الذي كف أيديهم عنكم وأيديكم عنهم ببطن مكة من بعد أن﴾ [الفَتح: 24]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo Iye ndi amene adatsekereza manja awo pa inu; ndi manja anu pa iwo, pa chigwa cha Makka, pambuyo pokupambanitsani pa iwo. Ndipo Allah akuona zonse zimene mukuchita
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek