×

oh inu anthu akhulupirira! Pewani kukaikirana chifukwa kukhala ndi chikayiko ndi tchimo. 49:12 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hujurat ⮕ (49:12) ayat 12 in Chichewa

49:12 Surah Al-hujurat ayat 12 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hujurat ayat 12 - الحُجُرَات - Page - Juz 26

﴿يَٰٓأَيُّهَا ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ ٱجۡتَنِبُواْ كَثِيرٗا مِّنَ ٱلظَّنِّ إِنَّ بَعۡضَ ٱلظَّنِّ إِثۡمٞۖ وَلَا تَجَسَّسُواْ وَلَا يَغۡتَب بَّعۡضُكُم بَعۡضًاۚ أَيُحِبُّ أَحَدُكُمۡ أَن يَأۡكُلَ لَحۡمَ أَخِيهِ مَيۡتٗا فَكَرِهۡتُمُوهُۚ وَٱتَّقُواْ ٱللَّهَۚ إِنَّ ٱللَّهَ تَوَّابٞ رَّحِيمٞ ﴾
[الحُجُرَات: 12]

oh inu anthu akhulupirira! Pewani kukaikirana chifukwa kukhala ndi chikayiko ndi tchimo. Ndipo musachite ukazitape pakati panu kapena amiseche. Kodi wina wa inu angakondwere kudya mnofu wa mnzake amene ndi wakufa? Kodi koma inu mumakana kudya.. Kotero opani Mulungu. Ndithudi Mulungu amabwezera chisoni chifukwa ndiye Mwini Chisoni Chosatha

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأيها الذين آمنوا اجتنبوا كثيرا من الظن إن بعض الظن إثم ولا, باللغة نيانجا

﴿ياأيها الذين آمنوا اجتنبوا كثيرا من الظن إن بعض الظن إثم ولا﴾ [الحُجُرَات: 12]

Khaled Ibrahim Betala
“E inu amene mwakhulupirira! Dzitalikitseni kuwaganizira kwambiri zoipa (anthu abwino). Ndithu kuganizira (anthu) maganizo (oipa) nditchimo. Ndipo musafufuzefufuze (nkhani za anthu) ndiponso musajedane pakati panu. Kodi mmodzi wa inu angakonde kudya minofu ya m’bale wake wakufa? Simungakonde zimenezo ndipo muopeni Allah. Ndithu Allah Ngolandira kulapa, Ngwachisoni chosatha
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek