×

oh inu anthu a m’Buku! Ndithudi Mtumwi wathu wadza kudzakuuzani inu zambiri 5:15 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:15) ayat 15 in Chichewa

5:15 Surah Al-Ma’idah ayat 15 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 15 - المَائدة - Page - Juz 6

﴿يَٰٓأَهۡلَ ٱلۡكِتَٰبِ قَدۡ جَآءَكُمۡ رَسُولُنَا يُبَيِّنُ لَكُمۡ كَثِيرٗا مِّمَّا كُنتُمۡ تُخۡفُونَ مِنَ ٱلۡكِتَٰبِ وَيَعۡفُواْ عَن كَثِيرٖۚ قَدۡ جَآءَكُم مِّنَ ٱللَّهِ نُورٞ وَكِتَٰبٞ مُّبِينٞ ﴾
[المَائدة: 15]

oh inu anthu a m’Buku! Ndithudi Mtumwi wathu wadza kudzakuuzani inu zambiri zimene mwakhala mukuzibisa za m’Buku la Mulungu ndi kuzisiya osafotokoza bwino. Ndithudi kwadza kuwala kwa inu kuchokera kwa Mulungu ndi Buku la choonadi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأهل الكتاب قد جاءكم رسولنا يبين لكم كثيرا مما كنتم تخفون من, باللغة نيانجا

﴿ياأهل الكتاب قد جاءكم رسولنا يبين لكم كثيرا مما كنتم تخفون من﴾ [المَائدة: 15]

Khaled Ibrahim Betala
“E inu anthu a buku! Ndithudi wakufikani Mtumiki Wathu yemwe akukufotokozerani poyera zambiri zomwe munkabisa za m’buku. Koma akusiya zambiri (posazilongosola). Ndithudi kwakudzerani kuunika kochokera kwa Allah ndi buku lomwe likufotokoza mwatchutchutchu (chinthu chilichonse)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek