×

Nena: “oh inu anthu a m’Buku! Inu mulibe poimira mpaka pamene mutatsatira 5:68 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:68) ayat 68 in Chichewa

5:68 Surah Al-Ma’idah ayat 68 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 68 - المَائدة - Page - Juz 6

﴿قُلۡ يَٰٓأَهۡلَ ٱلۡكِتَٰبِ لَسۡتُمۡ عَلَىٰ شَيۡءٍ حَتَّىٰ تُقِيمُواْ ٱلتَّوۡرَىٰةَ وَٱلۡإِنجِيلَ وَمَآ أُنزِلَ إِلَيۡكُم مِّن رَّبِّكُمۡۗ وَلَيَزِيدَنَّ كَثِيرٗا مِّنۡهُم مَّآ أُنزِلَ إِلَيۡكَ مِن رَّبِّكَ طُغۡيَٰنٗا وَكُفۡرٗاۖ فَلَا تَأۡسَ عَلَى ٱلۡقَوۡمِ ٱلۡكَٰفِرِينَ ﴾
[المَائدة: 68]

Nena: “oh inu anthu a m’Buku! Inu mulibe poimira mpaka pamene mutatsatira Buku la chipangano chakale ndi chipangano chatsopano ndi zimene zavumbulutsidwa kwa inu kuchokera kwa Ambuye wanu.” Ndithudi zimene zavumbulutsidwa kwa iwe kuchokera kwa Ambuye wako ziwonjezera, mwa ambiri a iwo, machimo ndi kusakhulupirira. Motero iwe usamve chisoni ndi anthu osakhulupirira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل ياأهل الكتاب لستم على شيء حتى تقيموا التوراة والإنجيل وما أنـزل, باللغة نيانجا

﴿قل ياأهل الكتاب لستم على شيء حتى تقيموا التوراة والإنجيل وما أنـزل﴾ [المَائدة: 68]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena: “E inu anthu a buku! Simuli kanthu (pa chipembedzo chanu) mpaka muimilire (kutsatira malamulo) a Taurat ndi Injili ndi zomwe zavumbulutsidwa kwa inu kuchokera kwa Mbuye wanu, ziwaonjezera kulakwa ndi kusakhulupirira ambiri a iwo zomwe zavumbulutsidwa kwa iwe kuchokera kwa Mbuye wako, choncho usadandaule za anthu osakhulupirira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek