Quran with Chichewa translation - Surah Qaf ayat 27 - قٓ - Page - Juz 26
﴿۞ قَالَ قَرِينُهُۥ رَبَّنَا مَآ أَطۡغَيۡتُهُۥ وَلَٰكِن كَانَ فِي ضَلَٰلِۭ بَعِيدٖ ﴾
[قٓ: 27]
﴿قال قرينه ربنا ما أطغيته ولكن كان في ضلال بعيد﴾ [قٓ: 27]
Khaled Ibrahim Betala “Mnzake (satana) adzanena: “E Mbuye wathu! Sindidamsokeretse, koma iye mwini adali wosokera kutali kwambiri ndi choonadi” |