×

Patsiku limene amuna a chinyengo ndi akazi a chinyengo adzanena kwa iwo 57:13 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hadid ⮕ (57:13) ayat 13 in Chichewa

57:13 Surah Al-hadid ayat 13 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hadid ayat 13 - الحدِيد - Page - Juz 27

﴿يَوۡمَ يَقُولُ ٱلۡمُنَٰفِقُونَ وَٱلۡمُنَٰفِقَٰتُ لِلَّذِينَ ءَامَنُواْ ٱنظُرُونَا نَقۡتَبِسۡ مِن نُّورِكُمۡ قِيلَ ٱرۡجِعُواْ وَرَآءَكُمۡ فَٱلۡتَمِسُواْ نُورٗاۖ فَضُرِبَ بَيۡنَهُم بِسُورٖ لَّهُۥ بَابُۢ بَاطِنُهُۥ فِيهِ ٱلرَّحۡمَةُ وَظَٰهِرُهُۥ مِن قِبَلِهِ ٱلۡعَذَابُ ﴾
[الحدِيد: 13]

Patsiku limene amuna a chinyengo ndi akazi a chinyengo adzanena kwa iwo okhulupirira:“Tidikirirenikutitikhozakulandirachilangali kuchokera ku muuni wanu.” Koma kudzanenedwa kuti: “Bwererani m’mbuyo kuti mukafune muuni wanu. Ndipo chipupa chidzakhazikitsidwa pakati pawo chokhala ndi khomo. Mbali ina ya chipupachi kudzakhala chisomo pamene mbali ina kudzakhala chilango.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: يوم يقول المنافقون والمنافقات للذين آمنوا انظرونا نقتبس من نوركم قيل ارجعوا, باللغة نيانجا

﴿يوم يقول المنافقون والمنافقات للذين آمنوا انظرونا نقتبس من نوركم قيل ارجعوا﴾ [الحدِيد: 13]

Khaled Ibrahim Betala
“Tsiku limene achinyengo aamuna ndi achinyengo aakazi adzauza okhulupirira (kuti:) “Tidikireni kuti tipeze kuunika kwanu!” Kudzanenedwa (mwachipongwe): “Bwererani pambuyo panu mukafune kuunika kumeneko!” Choncho padzaikidwa mpanda pakati pawo (okhulupirira ndi achinyengo) umene udzakhala ndi khomo, mkati mwake muli chifundo ndi mtendere; kunja kwake kuli mazunzo ndi chilango
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek