×

Iwo adzalira kwa iwo. “Kodi inu sitinali kukhalira limodzi?” Okhulupilira adzayankha kuti: 57:14 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hadid ⮕ (57:14) ayat 14 in Chichewa

57:14 Surah Al-hadid ayat 14 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hadid ayat 14 - الحدِيد - Page - Juz 27

﴿يُنَادُونَهُمۡ أَلَمۡ نَكُن مَّعَكُمۡۖ قَالُواْ بَلَىٰ وَلَٰكِنَّكُمۡ فَتَنتُمۡ أَنفُسَكُمۡ وَتَرَبَّصۡتُمۡ وَٱرۡتَبۡتُمۡ وَغَرَّتۡكُمُ ٱلۡأَمَانِيُّ حَتَّىٰ جَآءَ أَمۡرُ ٱللَّهِ وَغَرَّكُم بِٱللَّهِ ٱلۡغَرُورُ ﴾
[الحدِيد: 14]

Iwo adzalira kwa iwo. “Kodi inu sitinali kukhalira limodzi?” Okhulupilira adzayankha kuti: “Zoonadi koma inu mudadzisocheretsa nokha. Inu mudanyengedwa, mudakayikira ndipo zilakolako zanu zidakunyengani inu mpaka pamene chilango cha Mulungu chinachitika. Ndipo wonyenga adakunyengani inu pa nkhani zokhudza Mulungu.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ينادونهم ألم نكن معكم قالوا بلى ولكنكم فتنتم أنفسكم وتربصتم وارتبتم وغرتكم, باللغة نيانجا

﴿ينادونهم ألم نكن معكم قالوا بلى ولكنكم فتنتم أنفسكم وتربصتم وارتبتم وغرتكم﴾ [الحدِيد: 14]

Khaled Ibrahim Betala
“(Achinyengo) adzaitana okhulupirira ponena kuti: “Kodi sitidali nanu limodzi (pa dziko ndi kumatsagana nanu?” (Okhulupirira) adzati: “Inde! (Mudali nafe monga momwe mukunenera). Koma inu munadziononga nokha ndipo mumayembekezera (kuti okhulupirira awapeze mavuto ndi kuonongeka); mudakaikira (zinthu za chilengedwe chanu); choncho zikhulupiliro zanu zonama zidakunyengani pomwe mudali angwiro mpaka lamulo la Allah (imfa) lidakupezani, komanso adakunyengani onyenga (satana) za Allah
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek