×

Oh inu anthu okhulupirira! Ngati muuzidwa kukonza malo m’misonkhano yanu, konzani malo 58:11 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Mujadilah ⮕ (58:11) ayat 11 in Chichewa

58:11 Surah Al-Mujadilah ayat 11 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Mujadilah ayat 11 - المُجَادلة - Page - Juz 28

﴿يَٰٓأَيُّهَا ٱلَّذِينَ ءَامَنُوٓاْ إِذَا قِيلَ لَكُمۡ تَفَسَّحُواْ فِي ٱلۡمَجَٰلِسِ فَٱفۡسَحُواْ يَفۡسَحِ ٱللَّهُ لَكُمۡۖ وَإِذَا قِيلَ ٱنشُزُواْ فَٱنشُزُواْ يَرۡفَعِ ٱللَّهُ ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ مِنكُمۡ وَٱلَّذِينَ أُوتُواْ ٱلۡعِلۡمَ دَرَجَٰتٖۚ وَٱللَّهُ بِمَا تَعۡمَلُونَ خَبِيرٞ ﴾
[المُجَادلة: 11]

Oh inu anthu okhulupirira! Ngati muuzidwa kukonza malo m’misonkhano yanu, konzani malo okwanira. Ndipo Mulungu adzakukonzerani inu malo okwanira kwambiri. Ndipo mukauzidwa kuti mudzuke, dzukani. Mulungu adzakweza mu maudindo ena a inu amene mukhulupirira ndi iwo amene apatsidwa nzeru. Ndipo Mulungu amadziwa ntchito zanu zonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأيها الذين آمنوا إذا قيل لكم تفسحوا في المجالس فافسحوا يفسح الله, باللغة نيانجا

﴿ياأيها الذين آمنوا إذا قيل لكم تفسحوا في المجالس فافسحوا يفسح الله﴾ [المُجَادلة: 11]

Khaled Ibrahim Betala
“E inu amene mwakhulupirira! Kukapemphedwa kwa inu kuti perekani malo pabwalo (pokhala), perekani malowo (kuti anzanu apeze pokhala; mukatero) Allah akuphanulirani (chifundo Chake pano pa dziko ndi kumwamba). Ndipo kukanenedwa kuti imilirani, muimilire (musanyozere, apatseni ena malo); Allah awakwezera (ulemelero) mwa inu amene akhulupirira ndi amene apatsidwa nzeru. Ndipo Allah akudziwa bwino zimene mukuchita
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek