×

Iwo amene ali pakati panu ndipo amasudzula akazi awo ponena kuti: “Iwe 58:2 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Mujadilah ⮕ (58:2) ayat 2 in Chichewa

58:2 Surah Al-Mujadilah ayat 2 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Mujadilah ayat 2 - المُجَادلة - Page - Juz 28

﴿ٱلَّذِينَ يُظَٰهِرُونَ مِنكُم مِّن نِّسَآئِهِم مَّا هُنَّ أُمَّهَٰتِهِمۡۖ إِنۡ أُمَّهَٰتُهُمۡ إِلَّا ٱلَّٰٓـِٔي وَلَدۡنَهُمۡۚ وَإِنَّهُمۡ لَيَقُولُونَ مُنكَرٗا مِّنَ ٱلۡقَوۡلِ وَزُورٗاۚ وَإِنَّ ٱللَّهَ لَعَفُوٌّ غَفُورٞ ﴾
[المُجَادلة: 2]

Iwo amene ali pakati panu ndipo amasudzula akazi awo ponena kuti: “Iwe uli ngati msana wa Amai anga.” Iwo sangakhale Amai awo ai. Palibe amene angakhale amayi awo, kupatula okhawo amene anawabara. Ndithudi iwo amalankhula mau oipa ndi bodza. Ndithudi Mulungu amakhululukira nthawi zonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: الذين يظاهرون منكم من نسائهم ما هن أمهاتهم إن أمهاتهم إلا اللائي, باللغة نيانجا

﴿الذين يظاهرون منكم من نسائهم ما هن أمهاتهم إن أمهاتهم إلا اللائي﴾ [المُجَادلة: 2]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek