×

Ndipo iwo amene amasudzula akazi ponena kuti amaoneka ngati kumbuyo kwa amayi 58:3 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Mujadilah ⮕ (58:3) ayat 3 in Chichewa

58:3 Surah Al-Mujadilah ayat 3 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Mujadilah ayat 3 - المُجَادلة - Page - Juz 28

﴿وَٱلَّذِينَ يُظَٰهِرُونَ مِن نِّسَآئِهِمۡ ثُمَّ يَعُودُونَ لِمَا قَالُواْ فَتَحۡرِيرُ رَقَبَةٖ مِّن قَبۡلِ أَن يَتَمَآسَّاۚ ذَٰلِكُمۡ تُوعَظُونَ بِهِۦۚ وَٱللَّهُ بِمَا تَعۡمَلُونَ خَبِيرٞ ﴾
[المُجَادلة: 3]

Ndipo iwo amene amasudzula akazi ponena kuti amaoneka ngati kumbuyo kwa amayi awo kenaka afuna kuti akhululukidwe pa zomwe adanena ayenera kumasula kapolo asanabwererane. Limeneli ndi lamulo limene mwalamulidwa kuti mulimvere ndipo Mulungu amadziwa chilichonse chimene mumachita

❮ Previous Next ❯

ترجمة: والذين يظاهرون من نسائهم ثم يعودون لما قالوا فتحرير رقبة من قبل, باللغة نيانجا

﴿والذين يظاهرون من نسائهم ثم يعودون لما قالوا فتحرير رقبة من قبل﴾ [المُجَادلة: 3]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek