×

oh inu okhulupirira! Khalani otumikira Mulungu monga momwe ananenera Yesu, mwana wa 61:14 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah As-saff ⮕ (61:14) ayat 14 in Chichewa

61:14 Surah As-saff ayat 14 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah As-saff ayat 14 - الصَّف - Page - Juz 28

﴿يَٰٓأَيُّهَا ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ كُونُوٓاْ أَنصَارَ ٱللَّهِ كَمَا قَالَ عِيسَى ٱبۡنُ مَرۡيَمَ لِلۡحَوَارِيِّـۧنَ مَنۡ أَنصَارِيٓ إِلَى ٱللَّهِۖ قَالَ ٱلۡحَوَارِيُّونَ نَحۡنُ أَنصَارُ ٱللَّهِۖ فَـَٔامَنَت طَّآئِفَةٞ مِّنۢ بَنِيٓ إِسۡرَٰٓءِيلَ وَكَفَرَت طَّآئِفَةٞۖ فَأَيَّدۡنَا ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ عَلَىٰ عَدُوِّهِمۡ فَأَصۡبَحُواْ ظَٰهِرِينَ ﴾
[الصَّف: 14]

oh inu okhulupirira! Khalani otumikira Mulungu monga momwe ananenera Yesu, mwana wa mwamuna wa Maria, kwa ophunzira ake: “Kodi ndani andithandiza ine potumikira Mulungu?” Iwo adayankha: “Ife ndife othandiza Mulungu.” Kotero ena mwa ana a Israyeli adakhulupirira pamene ena sadakhulupirire. Motero Ife tidawapatsa mphamvu iwo amene adakhulupirira zopambana adani awo ndipo iwo adapambanadi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأيها الذين آمنوا كونوا أنصار الله كما قال عيسى ابن مريم للحواريين, باللغة نيانجا

﴿ياأيها الذين آمنوا كونوا أنصار الله كما قال عيسى ابن مريم للحواريين﴾ [الصَّف: 14]

Khaled Ibrahim Betala
“E inu amene mwakhulupirira! Khalani othangata (kufalitsa chipembedzo cha) Allah (pamene Mtumiki akukuitanani kuti mumthangate) monga momwe adanenera Isa (Yesu) mwana wa Mariya powauza otsatira ake: “Ndani adzandithangata pa ntchito ya Allah (yofalitsa chipembedzo Chake)? Otsatira ake adanena: “Ife ndife othangata (kufalitsa chipembedzo cha) Allah.” Choncho gulu lina la ana a Israyeli lidakhululupirira, ndipo gulu lina silidakhululupirire, tero tidawapatsa mphamvu amene adakhulupirira pa adani awo, ndipo adali opambana
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek