×

Patsiku limene Iye adzakusonkhanitsani inu nonse, tsiku losonkhana, tsiku limeneli lidzakhala tsiku 64:9 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taghabun ⮕ (64:9) ayat 9 in Chichewa

64:9 Surah At-Taghabun ayat 9 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taghabun ayat 9 - التغَابُن - Page - Juz 28

﴿يَوۡمَ يَجۡمَعُكُمۡ لِيَوۡمِ ٱلۡجَمۡعِۖ ذَٰلِكَ يَوۡمُ ٱلتَّغَابُنِۗ وَمَن يُؤۡمِنۢ بِٱللَّهِ وَيَعۡمَلۡ صَٰلِحٗا يُكَفِّرۡ عَنۡهُ سَيِّـَٔاتِهِۦ وَيُدۡخِلۡهُ جَنَّٰتٖ تَجۡرِي مِن تَحۡتِهَا ٱلۡأَنۡهَٰرُ خَٰلِدِينَ فِيهَآ أَبَدٗاۚ ذَٰلِكَ ٱلۡفَوۡزُ ٱلۡعَظِيمُ ﴾
[التغَابُن: 9]

Patsiku limene Iye adzakusonkhanitsani inu nonse, tsiku losonkhana, tsiku limeneli lidzakhala tsiku la mavuto ndi la mtendere kwa ena a inu. Ndipo iwo amene amakhulupirira mwa Mulungu ndipo amachita ntchito zabwino, Iye adzawakhululukira machimo awo ndipo adzawaika m’minda imene imathiriridwa ndi mitsinje yoyenda madzi pansi pake kuti akhale m’menemo mpaka kalekale. Kumeneko ndiko kupambana kwenikweni

❮ Previous Next ❯

ترجمة: يوم يجمعكم ليوم الجمع ذلك يوم التغابن ومن يؤمن بالله ويعمل صالحا, باللغة نيانجا

﴿يوم يجمعكم ليوم الجمع ذلك يوم التغابن ومن يؤمن بالله ويعمل صالحا﴾ [التغَابُن: 9]

Khaled Ibrahim Betala
“(Kumbukirani) tsiku limene adzakusonkhanitsani chifukwa cha tsiku lakusonkhana (zolengedwa zonse), limenelo ndi tsiku lolephera; ndipo amene akhulupirira mwa Allah ndi kuchita zabwino, amfafanizira zoipa zake, ndipo akamulowetsa m’minda momwe pansi pake pakuyenda mitsinje; adzakhala m’menemo muyaya; kumeneko ndiko kupambana kwakukulu
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek