×

Khalani nawo monga momwe inu muli kukhalira, molingana ndi kupeza kwanu. Musawazunze 65:6 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah AT-Talaq ⮕ (65:6) ayat 6 in Chichewa

65:6 Surah AT-Talaq ayat 6 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah AT-Talaq ayat 6 - الطَّلَاق - Page - Juz 28

﴿أَسۡكِنُوهُنَّ مِنۡ حَيۡثُ سَكَنتُم مِّن وُجۡدِكُمۡ وَلَا تُضَآرُّوهُنَّ لِتُضَيِّقُواْ عَلَيۡهِنَّۚ وَإِن كُنَّ أُوْلَٰتِ حَمۡلٖ فَأَنفِقُواْ عَلَيۡهِنَّ حَتَّىٰ يَضَعۡنَ حَمۡلَهُنَّۚ فَإِنۡ أَرۡضَعۡنَ لَكُمۡ فَـَٔاتُوهُنَّ أُجُورَهُنَّ وَأۡتَمِرُواْ بَيۡنَكُم بِمَعۡرُوفٖۖ وَإِن تَعَاسَرۡتُمۡ فَسَتُرۡضِعُ لَهُۥٓ أُخۡرَىٰ ﴾
[الطَّلَاق: 6]

Khalani nawo monga momwe inu muli kukhalira, molingana ndi kupeza kwanu. Musawazunze ndi cholinga chowasowetsa mtendere. Ngati iwo ali ndi pakati, asamalireni mpaka pamene iwo abereka. Ndipo ngati iwo ali kuyamwitsa, apatseni malipiro awo ndipo lemekezanani. Ndipo ngati pali mavuto oti simuli kugwirizana m’banja, pezani Mayi wina kuti ayamwitse mwana m’malo mwake

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أسكنوهن من حيث سكنتم من وجدكم ولا تضاروهن لتضيقوا عليهن وإن كن, باللغة نيانجا

﴿أسكنوهن من حيث سكنتم من وجدكم ولا تضاروهن لتضيقوا عليهن وإن كن﴾ [الطَّلَاق: 6]

Khaled Ibrahim Betala
“Akhazikeni (osiyidwawo) m’mene mukukhala inumo monga momwe kulili kupeza kwanu (ndi mphamvu zanu ngakhale kuti mwawasiya ukwati). Musawavute ndi cholinga chowapana (kuti athawe okha). Ngati ali ndi pakati, apatseni zonse zofunika pa moyo mpaka adzabereke. Ngati akukuyamwitsirani ana anu apatseni malipiro awo mokwanira; gwirizanani pakati panu mwa ubwino ndi mofatsa. Ngati wina apereka mavuto kwa mnzake (ndiye kuti mwanayo) adzamuyamwitsira (mkazi) wina
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek