×

Iye amene adalenga imfa ndi moyo kuti akhoza kukuyesani inu kuti ndani 67:2 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Mulk ⮕ (67:2) ayat 2 in Chichewa

67:2 Surah Al-Mulk ayat 2 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Mulk ayat 2 - المُلك - Page - Juz 29

﴿ٱلَّذِي خَلَقَ ٱلۡمَوۡتَ وَٱلۡحَيَوٰةَ لِيَبۡلُوَكُمۡ أَيُّكُمۡ أَحۡسَنُ عَمَلٗاۚ وَهُوَ ٱلۡعَزِيزُ ٱلۡغَفُورُ ﴾
[المُلك: 2]

Iye amene adalenga imfa ndi moyo kuti akhoza kukuyesani inu kuti ndani wa inu amene wasunga malamulo onse mwaubwino. Ndipo Iye ndi Wamphamvu ndi Wokhululukira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: الذي خلق الموت والحياة ليبلوكم أيكم أحسن عملا وهو العزيز الغفور, باللغة نيانجا

﴿الذي خلق الموت والحياة ليبلوكم أيكم أحسن عملا وهو العزيز الغفور﴾ [المُلك: 2]

Khaled Ibrahim Betala
“Amene adalenga imfa ndi moyo kuti akuyeseni (mayeso) ndani mwa inu ali wochita zabwino (kwambiri). Ndipo Iye ndiWopambana m’mphamvu (salephera kanthu) ndiponso Wokhululukira (olakwa)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek