×

Kodi ndani amene angakupatseni chisamaliro ngati Iye atakaniza chisamaliro chake? Koma iwo 67:21 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Mulk ⮕ (67:21) ayat 21 in Chichewa

67:21 Surah Al-Mulk ayat 21 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Mulk ayat 21 - المُلك - Page - Juz 29

﴿أَمَّنۡ هَٰذَا ٱلَّذِي يَرۡزُقُكُمۡ إِنۡ أَمۡسَكَ رِزۡقَهُۥۚ بَل لَّجُّواْ فِي عُتُوّٖ وَنُفُورٍ ﴾
[المُلك: 21]

Kodi ndani amene angakupatseni chisamaliro ngati Iye atakaniza chisamaliro chake? Koma iwo amapitiriza kuchita mtudzu ndi kugalukira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أمن هذا الذي يرزقكم إن أمسك رزقه بل لجوا في عتو ونفور, باللغة نيانجا

﴿أمن هذا الذي يرزقكم إن أمسك رزقه بل لجوا في عتو ونفور﴾ [المُلك: 21]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi ndani uyo amene angakupatseni rizq (limene mungakhalire ndi moyo ndi kupezera mtendere) ngati Iye atatsekereza rizq Lake (kwa inu)? Koma Akafiri akupitiriza kudzikweza kwawo, ndi kudziika kutali ndi choonadi
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek