×

Kodi m’badwo uno, umene wadza pambuyo pa wina, siuzindikira kuti ngati Ife 7:100 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:100) ayat 100 in Chichewa

7:100 Surah Al-A‘raf ayat 100 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 100 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿أَوَلَمۡ يَهۡدِ لِلَّذِينَ يَرِثُونَ ٱلۡأَرۡضَ مِنۢ بَعۡدِ أَهۡلِهَآ أَن لَّوۡ نَشَآءُ أَصَبۡنَٰهُم بِذُنُوبِهِمۡۚ وَنَطۡبَعُ عَلَىٰ قُلُوبِهِمۡ فَهُمۡ لَا يَسۡمَعُونَ ﴾
[الأعرَاف: 100]

Kodi m’badwo uno, umene wadza pambuyo pa wina, siuzindikira kuti ngati Ife titafuna, tikhoza kuulanga chifukwa cha machimo awo? Ndipo timaika chimatiro m’mitima mwawo kuti asamve

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أو لم يهد للذين يرثون الأرض من بعد أهلها أن لو نشاء, باللغة نيانجا

﴿أو لم يهد للذين يرثون الأرض من بعد أهلها أن لو نشاء﴾ [الأعرَاف: 100]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi sadadziwe awa omwe alandira dziko molowa mmalo pambuyo pa eni dzikolo (anthu akale) kuti tikadafuna tikadawaika m’masautso chifukwa cha machimo awo ndi kuwadinda mitima yawo kotero iwo sakadamva (kanthu)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek