×

Ndi pamene tidakweza phiri ndikuliika pamwamba pawo kukhala ngati mthunzi ndipo iwo 7:171 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:171) ayat 171 in Chichewa

7:171 Surah Al-A‘raf ayat 171 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 171 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿۞ وَإِذۡ نَتَقۡنَا ٱلۡجَبَلَ فَوۡقَهُمۡ كَأَنَّهُۥ ظُلَّةٞ وَظَنُّوٓاْ أَنَّهُۥ وَاقِعُۢ بِهِمۡ خُذُواْ مَآ ءَاتَيۡنَٰكُم بِقُوَّةٖ وَٱذۡكُرُواْ مَا فِيهِ لَعَلَّكُمۡ تَتَّقُونَ ﴾
[الأعرَاف: 171]

Ndi pamene tidakweza phiri ndikuliika pamwamba pawo kukhala ngati mthunzi ndipo iwo amaganiza kuti liwagwera. Ndipo Ife tidati, “Gwiritsani chimene takupatsani inu ndipo kumbukirani zimene zili m’kati mwake kuti mukhale oopa Mulungu ndi kumumvera Iye.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإذ نتقنا الجبل فوقهم كأنه ظلة وظنوا أنه واقع بهم خذوا ما, باللغة نيانجا

﴿وإذ نتقنا الجبل فوقهم كأنه ظلة وظنوا أنه واقع بهم خذوا ما﴾ [الأعرَاف: 171]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo(akumbutse) pamene tidalizula phiri ndikulinyamula pamwamba pawo monga denga (kapena mtambo umene wawavindikira) natsimikiza kuti liwagwera, (tidawauza): “Landirani, mwamphamvu malamulo amene takupatsani, ndipo kumbukirani zomwe zili m’menemo (pozitsata ndi kuzichita); kuti inu muope.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek